Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 16:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Inenso ndikanatha kulankhula ngati mmene mukuchitiramu,

      Moyo wanu ukanakhala ngati mmene ulili moyo wanga,

      Kodi ndikanalankhula mawu ogometsa okunenani?+

      Ndipo kodi ndikanakupukusirani mutu?+

  • Salimo 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anthu onse ondiona amandinyodola.+

      Iwo amandinyogodola ndi pakamwa pawo, ndipo amapukusa mitu yawo mondinyoza.+ Iwo amati:

  • Salimo 109:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kwa iwo ndakhala chinthu choyenera kutonzedwa.+

      Akandiona amapukusa mitu yawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena