Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Musabweretsenso nsembe zina zaufa zopanda phindu.+ Zofukiza zanu ndikunyansidwa nazo.+ Mumasunga masiku okhala mwezi+ ndi sabata,+ ndipo mumaitanitsa misonkhano.+ Koma ine ndatopa kukuonani mukugwiritsira ntchito mphamvu zamatsenga+ pamene mukuchita misonkhano yapadera.

  • Amosi 5:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kodi anthu inu a m’nyumba ya Isiraeli, munandipatsa nsembe zanyama ndi zopereka zina pamene munali m’chipululu muja kwa zaka 40?+

  • Malaki 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Inu mumanena kuti, ‘Koma ndiye n’zotopetsa bwanji!’+ Ndipo mumanunkhiza nsembezo monyansidwa,” watero Yehova wa makamu. “Inu mumabweretsa nyama zobedwa, zolumala ndi zodwala.+ Mumapereka zimenezi ngati mphatso. Kodi zopereka zanu zoterezi ine ndingakondwere nazo?”+ watero Yehova.

  • Malaki 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Kodi munthu wochokera kufumbi angabere Mulungu? Komatu inu mukundibera.”

      Inu mukunena kuti: “Takuberani motani?”

      “Mukundibera kudzera m’chakhumi* ndi m’zopereka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena