Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kwa Adamu, Mulungu ananena kuti: “Chifukwa wamvera mawu a mkazi wako, ndipo wadya chipatso cha mtengo umene ndinakulamula+ kuti, ‘Usadzadye zipatso zake,’ nthaka ikhale yotembereredwa kwa iwe.+ Udzadya zotuluka m’nthakayo movutikira masiku onse a moyo wako.+

  • Salimo 78:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndipo asadzakhale ngati makolo awo,+

      M’badwo wosamva ndi wopanduka,+

      M’badwo umene sunakonze mtima wawo,+

      Ndipo maganizo awo sanali okhulupirika kwa Mulungu.+

  • Aroma 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiye chifukwa chake monga mmene uchimo unalowera m’dziko kudzera mwa munthu mmodzi,+ ndi imfa+ kudzera mwa uchimo, imfayo n’kufalikira kwa anthu onse chifukwa onse anachimwa+ . . .

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena