Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 102:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Zimenezi zidzatha, koma inu mudzakhalapobe.+

      Ndipo zonsezi zidzatha ngati chovala.+

      Mofanana ndi zovala zimene zatha, mudzapezerapo zina ndipo nazonso zidzatha.+

  • Yesaya 34:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Makamu onse akumwamba adzawola.+ Kumwamba kudzapindidwa ngati mpukutu wolembapo.+ Makamu onse akumwambawo adzafota ngati mmene masamba amafotera pamtengo wa mpesa n’kuthothoka, ndiponso ngati mmene nkhuyu yonyala imathothokera mumtengo wa mkuyu.+

  • Aheberi 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Zimenezi zidzatha, koma inu mudzakhalapo mpaka muyaya. Ndipo zonsezi zidzatha ngati mmene malaya akunja amathera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena