Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 74:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu Mulungu, kodi mdani adzakuchitirani mopanda ulemu kufikira liti?+

      Kodi mdani adzanyoza dzina lanu kwamuyaya?+

  • Yesaya 37:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno Yesaya anawauza kuti: “Mukauze mbuye wanu kuti, ‘Yehova wanena kuti:+ “Usachite mantha+ chifukwa cha mawu amene wamva, amene atumiki+ a mfumu ya Asuri andilankhulira monyoza.

  • Aroma 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pakuti “dzina la Mulungu likunyozedwa pakati pa anthu amitundu chifukwa cha inu”+ monga mmene Malemba amanenera.

  • Yakobo 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kodi si iwo amene amanyoza+ dzina labwino kwambiri limene mukuimira?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena