24 ndi kuvala+ umunthu watsopano+ umene unalengedwa+ mogwirizana ndi chifuniro cha Mulungu ndipo umatsatira zofunika pa chilungamo chenicheni+ ndi pa kukhulupirika.
9 Ndiponso kuti ndikapezeke wogwirizana ndi iye ndikuchita chilungamo. Osati chilungamo changachanga chobwera ndi chilamulo,+ koma chobwera mwa kukhulupirira+ Khristu, chochokera kwa Mulungu pa maziko a chikhulupiriro.+