Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 15:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Poyankha Samueli anati: “Kodi Yehova amakondwera ndi nsembe zopsereza+ ndi nsembe zina kuposa kumvera mawu a Yehova? Taona! Kumvera+ kuposa nsembe,+ ndipo kumvetsera mosamala kuposa mafuta+ a nkhosa zamphongo.

  • Salimo 40:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Nsembe ndiponso zopereka, simunasangalale nazo.+

      Inu munatsegula makutu anga.+

      Simunapemphe nsembe yopsereza ndi nsembe yamachimo.+

  • Salimo 51:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pakuti nsembe singakusangalatseni, chifukwa ikanakusangalatsani ndikanaipereka kwa inu.+

      Nsembe yopsereza yathunthu singakusangalatseni.+

  • Miyambo 15:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nsembe ya anthu oipa imam’nyansa Yehova,+ koma pemphero la anthu owongoka mtima limam’sangalatsa.+

  • Mateyu 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choncho pitani mukaphunzire tanthauzo la mawu akuti, ‘Ndikufuna chifundo, osati nsembe.’+ Chifukwa ine sindinabwere kudzaitana anthu olungama, koma ochimwa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena