Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 30:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Inu mudzakhaladi anthu anga+ ndipo ine ndidzakhala Mulungu wanu.”+

  • Yeremiya 32:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Iwo adzakhala anthu anga+ ndipo ine ndidzakhala Mulungu wawo.+

  • Ezekieli 14:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 kuti a nyumba ya Isiraeli asadzasiyenso kunditsatira n’kumangoyenda uku ndi uku,+ ndiponso kuti asadzadziipitsenso ndi zochimwa zawo zonse. Chotero iwo adzakhala anthu anga ndipo ine ndidzakhala Mulungu wawo,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”+

  • Zekariya 8:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndithu ndidzawabweretsa, ndipo adzakhala mu Yerusalemu.+ Iwo adzakhala anthu anga+ ndipo ine ndidzakhala Mulungu wawo woona ndi wachilungamo.’”+

  • Aheberi 8:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “‘Pangano limene ndidzapangana ndi nyumba ya Isiraeli pambuyo pa pangano loyamba lija ndi ili: Ndidzaika malamulo anga m’maganizo mwawo ndi kuwalemba m’mitima yawo.+ Ine ndidzakhala Mulungu wawo+ ndipo iwo adzakhala anthu anga,’+ watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena