Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 1:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Nthawi yomweyo Benaya mwana wa Yehoyada anayankha mfumu kuti: “Zikhale momwemo!*+ Yehova, Mulungu wa mbuyanga mfumu, atsimikizire zimenezi.+

  • Salimo 41:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Adalitsike Yehova Mulungu wa Isiraeli,+

      Kuyambira kalekale mpaka kalekale.+

      Ame! Ame!*+

  • Yeremiya 11:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 kuti ndikwaniritse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu+ kuti ndidzawapatsa dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ monga mmene zilili lero.’”’”

      Pamenepo ine ndinayankha kuti: “Zikhale momwemo,* inu Yehova.”

  • 2 Akorinto 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiponso malonjezo a Mulungu, kaya akhale ochuluka chotani,+ akhala Inde kudzera mwa iye.+ Choteronso kudzera mwa iye, “Ame”+ amanenedwa kwa Mulungu kuti Mulungu alandire ulemerero kudzera mwa ife.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena