1 Mbiri 17:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Choncho dalitsani nyumba ya mtumiki wanu kuti ikhazikike pamaso panu mpaka kalekale.+ Pakuti inu Yehova mwadalitsa nyumba ya mtumiki wanu, ndipo yadalitsika mpaka kalekale.”+ Yeremiya 11:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 kuti ndikwaniritse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu+ kuti ndidzawapatsa dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ monga mmene zilili lero.’”’” Pamenepo ine ndinayankha kuti: “Zikhale momwemo,* inu Yehova.” Yeremiya 28:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 inde, Yeremiya anayankha kuti: “Zikhale momwemo!*+ Yehova achitedi zimenezo! Yehova akwaniritse zonse zimene walosera m’mawu ako. Achite zimenezo mwa kubwezeretsa pamalo ano ziwiya za m’nyumba ya Yehova ndi anthu onse amene anatengedwa kupita ku ukapolo ku Babulo!+
27 Choncho dalitsani nyumba ya mtumiki wanu kuti ikhazikike pamaso panu mpaka kalekale.+ Pakuti inu Yehova mwadalitsa nyumba ya mtumiki wanu, ndipo yadalitsika mpaka kalekale.”+
5 kuti ndikwaniritse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu+ kuti ndidzawapatsa dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ monga mmene zilili lero.’”’” Pamenepo ine ndinayankha kuti: “Zikhale momwemo,* inu Yehova.”
6 inde, Yeremiya anayankha kuti: “Zikhale momwemo!*+ Yehova achitedi zimenezo! Yehova akwaniritse zonse zimene walosera m’mawu ako. Achite zimenezo mwa kubwezeretsa pamalo ano ziwiya za m’nyumba ya Yehova ndi anthu onse amene anatengedwa kupita ku ukapolo ku Babulo!+