Salimo 37:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Chilamulo cha Mulungu wake chili mumtima mwake.+Poyenda mapazi ake sadzaterereka.+ Aheberi 10:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 “‘Pangano limene ndidzapanga nawo pambuyo pa pangano loyamba lija ndi ili: Ndidzaika malamulo anga m’mitima yawo ndi kuwalemba m’maganizo mwawo,’ watero Yehova,”+
16 “‘Pangano limene ndidzapanga nawo pambuyo pa pangano loyamba lija ndi ili: Ndidzaika malamulo anga m’mitima yawo ndi kuwalemba m’maganizo mwawo,’ watero Yehova,”+