Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Koma iwe umange m’chiuno+ ndipo upite kukawauza zonse zimene ndikulamule kuti ukawauze. Usagwidwe ndi mantha chifukwa cha iwo,+ kuopera kuti ndingakuchititse kugwidwa ndi mantha pamaso pawo.

  • Yeremiya 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Yeremiya atamaliza kulankhula mawu onse amene Yehova anamulamula kuti akauze anthu onse, nthawi yomweyo ansembe, aneneri ndi anthu onse anamugwira ndi kunena kuti: “Ukufa basi.+

  • Yeremiya 42:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno iwo anauza Yeremiya kuti: “Yehova akhale mboni yoona ndi yokhulupirika, ndipo atilange+ ngati sitidzachita ndendende mogwirizana ndi mawu onse amene Yehova Mulungu wako angakutume kwa ife.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena