Deuteronomo 32:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Kubwezera ndi kwanga, chilangonso ndi changa.+Pa nthawi yoikidwiratu phazi lawo lidzaterereka poyenda,+Pakuti tsiku la tsoka lawo layandikira,+Ndipo zowagwera zikufika mofulumira.’+ Yesaya 16:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Koma tsopano Yehova wanena kuti: “Pomatha ndendende zaka zitatu,*+ ulemerero+ wa Mowabu udzatha. Iye adzachititsidwa manyazi ndipo adzakumana ndi chipwirikiti chamtundu uliwonse. Otsala mwa iye adzakhala ochepa kwambiri ndiponso opanda mphamvu.”+ Ezekieli 12:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Chotero iwe uwauze kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “‘Sindidzazengerezanso pa zimene ndalankhula.+ Mawu alionse amene ndalankhula adzakwaniritsidwadi,’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”’”+ Ezekieli 25:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndidzapereka chiweruzo m’dziko la Mowabu,+ ndipo adzadziwa kuti ine ndine Yehova.’+
35 Kubwezera ndi kwanga, chilangonso ndi changa.+Pa nthawi yoikidwiratu phazi lawo lidzaterereka poyenda,+Pakuti tsiku la tsoka lawo layandikira,+Ndipo zowagwera zikufika mofulumira.’+
14 Koma tsopano Yehova wanena kuti: “Pomatha ndendende zaka zitatu,*+ ulemerero+ wa Mowabu udzatha. Iye adzachititsidwa manyazi ndipo adzakumana ndi chipwirikiti chamtundu uliwonse. Otsala mwa iye adzakhala ochepa kwambiri ndiponso opanda mphamvu.”+
28 Chotero iwe uwauze kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “‘Sindidzazengerezanso pa zimene ndalankhula.+ Mawu alionse amene ndalankhula adzakwaniritsidwadi,’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”’”+