-
Yobu 9:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Kumwamba anakutambasula yekha,+
Ndipo amayenda pamafunde aatali a m’nyanja.+
-
Salimo 104:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Mwadzifunditsa kuwala ngati chofunda,+
Mwatambasula kumwamba ngati nsalu ya chihema.+
-
Salimo 136:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Yamikani amene anapanga kumwamba mwanzeru:+
Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+
-
-
-
-
-