Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Zingwe za imfa zinandikulunga,+

      Chikhamu cha anthu opanda pake chinali kundiopseza.+

  • Salimo 69:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndamila m’matope akuya, mmene mulibe malo oponda.+

      Ndalowa m’madzi akuya,

      Ndipo mtsinje wa madzi othamanga wandikokolola.+

  • Salimo 88:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Zandizungulira ngati madzi tsiku lonse.+

      Zandimiza pa nthawi imodzi.

  • Salimo 124:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Pamenepo madzi akanatikokolola,+

      Mtsinje wamphamvu ukanatimiza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena