-
Salimo 89:50Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
50 Inu Yehova, kumbukirani chitonzo chimene chagwera atumiki anu.+
Kumbukirani kuti ndanyamula pachifuwa panga chitonzo cha mitundu yambiri ya anthu.+
-