Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 “Ana a Aroni uwapangire mikanjo+ ndi malamba ake. Uwapangirenso mipango*+ yokulunga kumutu kuti iwapatse ulemerero ndi kuwakongoletsa.+

  • Ekisodo 29:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Ukatero utenge ana ake ndi kuwaveka mikanjo.+

  • Levitiko 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako Mose anaitana ana a Aroni+ ndi kuwaveka mikanjo, kuwamanga malamba a pamimba,+ ndi kuwakulunga mipango+ kumutu, monga mmene Yehova analamulira Mose.

  • Ezekieli 44:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Akafuna kupita kubwalo lakunja kumene kuli anthu, azivula zovala zawo zimene anavala potumikira.+ Aziika zovalazo m’zipinda zopatulika zodyeramo+ ndipo azivala zovala zina kuti asayeretse anthu ndi zovala zawozo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena