Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 N’chifukwa chake ndinudi wokwezeka,+ inu Yehova Ambuye Wamkulu Koposa. Ngakhale kuti tamva za milungu ina yambirimbiri, palibe Mulungu wina+ koma inu nokha.+

  • Salimo 96:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Pakuti Yehova ndi wamkulu+ ndi woyenera kutamandidwa kwambiri.

      Iye ndi wochititsa mantha kuposa milungu ina yonse.+

  • Salimo 145:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yehova ndi wamkulu ndi woyenera kutamandidwa kwambiri,+

      Ndipo ukulu wake ndi wosasanthulika.+

  • Yeremiya 32:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Inu mumasonyeza anthu masauzande ambiri kukoma mtima kosatha.+ Mumabwezera zolakwa za abambo kwa ana awo.*+ Inu ndinu Mulungu woona, wamkulu+ ndi wamphamvu,+ ndipo dzina lanu+ ndinu Yehova wa makamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena