16 Ndiyeno winawake wamaonekedwe ofanana ndi ana a anthu anakhudza milomo yanga.+ Atatero, ndinayamba kulankhula,+ ndipo ndinauza amene anali ataimirira patsogolo panga uja kuti: “Mbuyanga,+ ine ndinayamba kunjenjemera chifukwa cha zimene ndaona ndipo mphamvu zandithera.+