Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Thupi lake linali ngati mwala wa kulusolito,+ nkhope yake inali yowala ngati mphezi,+ maso ake anali kuoneka ngati miyuni yamoto,+ manja ake ndi mapazi ake zinali kuoneka ngati mkuwa wonyezimira,+ ndipo mawu ake anali kumveka ngati khamu la anthu.

  • Danieli 10:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno winawake wamaonekedwe ofanana ndi ana a anthu anakhudza milomo yanga.+ Atatero, ndinayamba kulankhula,+ ndipo ndinauza amene anali ataimirira patsogolo panga uja kuti: “Mbuyanga,+ ine ndinayamba kunjenjemera chifukwa cha zimene ndaona ndipo mphamvu zandithera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena