Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 2:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 “Ufumu wachinayi+ udzakhala wolimba ngati chitsulo.+ Popeza kuti chitsulo chimaphwanya ndi kupera china chilichonse, ufumuwo udzaphwanya ndi kuswa maufumu ena onsewa mofanana ndi chitsulo chimene chimaswa zinthu.+

  • Danieli 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Kenako ndinaonanso m’masomphenya ausiku chilombo chachinayi, choopsa kwambiri ndiponso chochititsa mantha komanso champhamvu kwambiri.+ Chinali ndi mano akuluakulu achitsulo ndipo chinali kudya ndi kuphwanyaphwanya chilichonse chimene chinali nacho pafupi. Zotsala chinali kuzipondaponda ndi mapazi ake. Chinali chosiyana ndi zilombo zina zonse zimene ndinaona poyamba ndipo chinali ndi nyanga 10.+

  • Danieli 7:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Ndiyeno ndinali ndi chidwi chofuna kudziwa zambiri zokhudza chilombo chachinayi chija, chimene chinali chosiyana ndi zina zonse. Chilombo chimenechi chinali choopsa kwambiri. Mano ake anali achitsulo, zikhadabo zake zinali zamkuwa, ndipo chinali kudya zinthu ndi kuziphwanyaphwanya. Zotsala chinali kuzipondaponda ndi mapazi ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena