Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 38:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndani amakonzera khwangwala chakudya,+

      Ana ake akamalirira Mulungu kuti awathandize,

      Akamadzandira chifukwa chosowa chakudya?

  • Salimo 147:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye amapatsa zilombo chakudya chawo,+

      Amapatsanso ana a makwangwala chakudya chimene amalirira.+

  • Mateyu 10:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kodi mpheta ziwiri si paja amazigulitsa kakhobidi kamodzi kochepa mphamvu?+ Komatu palibe ngakhale imodzi imene idzagwa pansi Atate wanu osadziwa.+

  • Luka 12:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Onetsetsani makwangwala,+ iwo safesa mbewu kapena kukolola. Alibe nyumba yosungiramo zinthu kapena nkhokwe, komatu Mulungu amawadyetsa. Kodi inu si ofunika kwambiri kuposa mbalame?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena