Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 35:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pa nthawi imeneyo, maso a anthu akhungu adzatsegulidwa,+ ndipo makutu a anthu ogontha adzayamba kumva.+

  • Mateyu 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Khamu lalikulu la anthu linam’tsatira, ndipo iye anawachiritsa kumeneko.+

  • Maliko 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Popeza kuti anali atachiritsa anthu ambiri, onse amene anali ndi matenda aakulu anali kudziponya kwa iye kuti angomukhudza.+

  • Maliko 7:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kumeneko anthu anam’bweretsera munthu wogontha komanso wovutika kulankhula. Iwo anamupempha kuti aike dzanja lake pa munthuyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena