Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Atadziwa zimenezi, Yesu anatuluka mmenemo. Anthu ambiri anam’tsatira ndipo iye anawachiritsa onsewo,+

  • Mateyu 14:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano Yesu atatsika m’ngalawayo anaona khamu lalikulu la anthu, ndipo anawamvera chisoni,+ ndi kuwachiritsira anthu awo odwala.+

  • Mateyu 15:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kenako anthu ochuluka anakhamukira kwa iye. Anabwera ndi anthu olumala, othyoka ziwalo, akhungu, osalankhula, ndi ena ambiri osiyanasiyana, moti anawakhazika pamapazi ake mochita ngati akum’ponyera, ndipo anawachiritsa onsewo.+

  • Luka 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma mbiri yake inali kufalikira kwambiri, ndipo makamu a anthu anali kusonkhana pamodzi kudzamumvetsera ndi kudzachiritsidwa matenda awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena