Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:99
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  99 Ndakhala wozindikira kwambiri kuposa aphunzitsi anga,+

      Chifukwa ndimasinkhasinkha zikumbutso zanu.+

  • Mateyu 7:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsopano Yesu atatsiriza mawu amenewa, khamu la anthulo linakhudzidwa moti linadabwa+ ndi kaphunzitsidwe kake,

  • Maliko 1:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mmenemo anthu anadabwa kwambiri ndi kaphunzitsidwe kake,+ chifukwa anali kuwaphunzitsa monga munthu wokhala ndi ulamuliro, osati monga alembi.+

  • Yohane 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo Ayudawo anayamba kudabwa ndi kufunsa kuti: “Kodi munthu ameneyu zolembazi anazidziwa bwanji,+ popeza sanapite kusukulu?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena