Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 9:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pakuti aliyense wochita manyazi ndi ine, komanso ndi mawu anga, Mwana wa munthu adzachitanso naye manyazi akadzafika mu ulemerero wake, wa Atate wake ndi wa angelo oyera.+

  • 2 Timoteyo 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tikapitiriza kupirira, tidzalamuliranso limodzi ndi iye monga mafumu.+ Tikamukana,+ iyenso adzatikana,

  • 1 Yohane 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Aliyense amene amakana Mwana sangakhale pa ubwenzi ndi Atate.+ Amene wavomereza+ Mwana amakhalanso pa ubwenzi ndi Atate.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena