Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma tsiku la 7 ndi sabata la Yehova Mulungu wanu.+ Musagwire ntchito iliyonse inuyo kapena mwana wanu wamwamuna, mwana wanu wamkazi, kapolo wanu wamwamuna, kapolo wanu wamkazi, chiweto chanu kapena mlendo wokhala mumzinda wanu.+

  • Nehemiya 13:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno mdima utafika pazipata za Yerusalemu, sabata lisanayambe, ndinapereka lamulo ndipo zitseko zinayamba kutsekedwa.+ Ndinalamulanso kuti asatsegule zitsekozo kufikira sabata litatha. Ndipo ndinaika ena mwa atumiki anga m’zipata kuti munthu asalowe ndi katundu tsiku la sabata.+

  • Yeremiya 17:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Yehova wanena kuti: “Samalani moyo wanu.+ Katundu aliyense amene mukufuna kulowa naye pazipata za Yerusalemu musamunyamule pa tsiku la sabata.+

  • Mateyu 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Afarisi ataona zimenezi anamuuza kuti:+ “Taona! Ophunzira ako akuchita zosayenera kuzichita pa sabata.”+

  • Luka 6:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Afarisi ena ataona zimenezi anati: “N’chifukwa chiyani mukuchita zosemphana ndi malamulo+ pa sabata?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena