15 Tsopano, inuyo pamodzi ndi Khoti Lalikulu la Ayuda, mufotokoze momveka bwino kwa mkulu wa asilikali. Mumuuze kuti amubweretse kwa inu, ngati kuti mukufuna kumvetsetsa bwino nkhani yokhudza munthu ameneyu.+ Koma asanafike n’komwe ife tidzakhala okonzeka kumupha.”+