Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsopano anthu okhala naye pafupi ndi anthu ena amene m’mbuyomo anali kumuona akupemphapempha anayamba kunena kuti: “Si uyu kodi amene anali kukhala pansi n’kumapemphapempha uja?”+

  • Machitidwe 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno tsiku ndi tsiku anthu anali kunyamula mwamuna wina amene anabadwa ali wolumala.+ Iwo anali kukhazika wolumalayo pafupi ndi khomo la kachisi lotchedwa Chipata Chokongola,+ kuti azipempha mphatso zachifundo kwa olowa m’kachisimo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena