Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 141:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pemphero langa likhale lokonzedwa ngati zofukiza+ pamaso panu,+

      Mapembedzero anga akhale ngati nsembe yambewu yamadzulo.+

  • Luka 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Khamu lonse la anthu linali kupemphera panja, pa ola lopereka nsembe zofukizalo.+

  • 1 Petulo 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma mapeto a zinthu zonse ayandikira.+ Choncho khalani oganiza bwino,+ ndipo khalani maso kuti musanyalanyaze kupemphera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena