Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 9
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 9:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:31; Yos 4:19
  • +De 4:38; 7:1; 11:23
  • +Nu 13:28

Deuteronomo 9:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 13:33; De 1:28; 2:21

Deuteronomo 9:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:30; 20:4; 31:3; Yos 3:11
  • +De 4:24; Nah 1:6; Ahe 12:29
  • +De 7:23; 20:16
  • +Eks 23:31; De 7:24

Deuteronomo 9:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:8; Eze 36:22
  • +Ge 15:16; De 12:31; 18:12

Deuteronomo 9:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 8:46; Sl 51:5; Aro 3:23; 5:12; Tit 3:5
  • +Yer 17:9
  • +Le 18:25
  • +Ge 13:15; 17:8
  • +Ge 26:3
  • +Ge 28:13

Deuteronomo 9:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:9; Sl 78:8; Yes 48:4; Mac 7:51

Deuteronomo 9:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 9:22; Sl 78:40; Ahe 3:16
  • +Eks 17:2; Nu 11:4; 16:2; 25:2; De 31:27; 32:5; Ne 9:16

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/1/1996, tsa. 30

Deuteronomo 9:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:4, 10; Sl 106:19

Deuteronomo 9:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:12; 31:18; 32:16
  • +Eks 24:7; Aga 4:24
  • +Eks 24:18

Deuteronomo 9:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 31:18; Sl 8:3; Mt 12:28; Lu 11:20
  • +Eks 19:19; De 4:10, 12

Deuteronomo 9:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 31:18; De 4:13

Deuteronomo 9:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:7; De 4:16
  • +Eks 32:4

Deuteronomo 9:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:9

Deuteronomo 9:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:10
  • +De 7:24; Sl 9:5
  • +Nu 14:12

Deuteronomo 9:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:18; De 4:11
  • +Eks 32:15

Deuteronomo 9:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 7:40
  • +Eks 20:3, 4; De 5:8; Mac 7:41

Deuteronomo 9:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:19

Deuteronomo 9:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:28
  • +Ne 9:18

Deuteronomo 9:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:10
  • +Eks 32:11, 14; De 10:10; Sl 106:23

Deuteronomo 9:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:2, 21, 35
  • +Miy 15:29; Yak 5:16

Deuteronomo 9:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 32:4
  • +Eks 32:20; Yes 30:22

Deuteronomo 9:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 11:3
  • +Eks 17:7; De 6:16
  • +Nu 11:4, 34
  • +De 9:7

Deuteronomo 9:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 13:26; De 1:19
  • +Nu 14:3, 4; Yes 63:10
  • +De 1:32; Sl 106:24; Ahe 3:19
  • +Sl 106:25

Deuteronomo 9:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:27; Mac 7:51

Deuteronomo 9:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:28; De 9:18; Mt 4:2
  • +De 9:19

Deuteronomo 9:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 99:6; Miy 15:29; Yak 5:16
  • +Eks 19:5; De 32:9; Sl 135:4; Amo 3:2
  • +1Mf 8:51
  • +Eks 32:11; Sl 99:6

Deuteronomo 9:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 3:6; 6:8; De 9:5
  • +Eks 32:31; Sl 78:8; Mik 7:18

Deuteronomo 9:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:6
  • +Eks 32:12; Nu 14:16; Sl 115:2

Deuteronomo 9:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:20; 1Mf 8:51; Ne 1:10; Sl 74:2; 95:7; 100:3
  • +Eks 6:6; De 4:34; Yes 63:12

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 9:1De 11:31; Yos 4:19
Deut. 9:1De 4:38; 7:1; 11:23
Deut. 9:1Nu 13:28
Deut. 9:2Nu 13:33; De 1:28; 2:21
Deut. 9:3De 1:30; 20:4; 31:3; Yos 3:11
Deut. 9:3De 4:24; Nah 1:6; Ahe 12:29
Deut. 9:3De 7:23; 20:16
Deut. 9:3Eks 23:31; De 7:24
Deut. 9:4De 7:8; Eze 36:22
Deut. 9:4Ge 15:16; De 12:31; 18:12
Deut. 9:51Mf 8:46; Sl 51:5; Aro 3:23; 5:12; Tit 3:5
Deut. 9:5Yer 17:9
Deut. 9:5Le 18:25
Deut. 9:5Ge 13:15; 17:8
Deut. 9:5Ge 26:3
Deut. 9:5Ge 28:13
Deut. 9:6Eks 34:9; Sl 78:8; Yes 48:4; Mac 7:51
Deut. 9:7De 9:22; Sl 78:40; Ahe 3:16
Deut. 9:7Eks 17:2; Nu 11:4; 16:2; 25:2; De 31:27; 32:5; Ne 9:16
Deut. 9:8Eks 32:4, 10; Sl 106:19
Deut. 9:9Eks 24:12; 31:18; 32:16
Deut. 9:9Eks 24:7; Aga 4:24
Deut. 9:9Eks 24:18
Deut. 9:10Eks 31:18; Sl 8:3; Mt 12:28; Lu 11:20
Deut. 9:10Eks 19:19; De 4:10, 12
Deut. 9:11Eks 31:18; De 4:13
Deut. 9:12Eks 32:7; De 4:16
Deut. 9:12Eks 32:4
Deut. 9:13Eks 32:9
Deut. 9:14Eks 32:10
Deut. 9:14De 7:24; Sl 9:5
Deut. 9:14Nu 14:12
Deut. 9:15Eks 19:18; De 4:11
Deut. 9:15Eks 32:15
Deut. 9:16Mac 7:40
Deut. 9:16Eks 20:3, 4; De 5:8; Mac 7:41
Deut. 9:17Eks 32:19
Deut. 9:18Eks 34:28
Deut. 9:18Ne 9:18
Deut. 9:19Eks 32:10
Deut. 9:19Eks 32:11, 14; De 10:10; Sl 106:23
Deut. 9:20Eks 32:2, 21, 35
Deut. 9:20Miy 15:29; Yak 5:16
Deut. 9:21Eks 32:4
Deut. 9:21Eks 32:20; Yes 30:22
Deut. 9:22Nu 11:3
Deut. 9:22Eks 17:7; De 6:16
Deut. 9:22Nu 11:4, 34
Deut. 9:22De 9:7
Deut. 9:23Nu 13:26; De 1:19
Deut. 9:23Nu 14:3, 4; Yes 63:10
Deut. 9:23De 1:32; Sl 106:24; Ahe 3:19
Deut. 9:23Sl 106:25
Deut. 9:24De 31:27; Mac 7:51
Deut. 9:25Eks 34:28; De 9:18; Mt 4:2
Deut. 9:25De 9:19
Deut. 9:26Sl 99:6; Miy 15:29; Yak 5:16
Deut. 9:26Eks 19:5; De 32:9; Sl 135:4; Amo 3:2
Deut. 9:261Mf 8:51
Deut. 9:26Eks 32:11; Sl 99:6
Deut. 9:27Eks 3:6; 6:8; De 9:5
Deut. 9:27Eks 32:31; Sl 78:8; Mik 7:18
Deut. 9:28De 5:6
Deut. 9:28Eks 32:12; Nu 14:16; Sl 115:2
Deut. 9:29De 4:20; 1Mf 8:51; Ne 1:10; Sl 74:2; 95:7; 100:3
Deut. 9:29Eks 6:6; De 4:34; Yes 63:12
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 9:1-29

Deuteronomo

9 “Tamverani Aisiraeli inu, lero mukuwoloka Yorodano+ kulowa m’dziko limene mukukalilanda kwa mitundu ikuluikulu ndi yamphamvu kuposa inuyo.+ Mukukalanda mizinda ikuluikulu yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri yofika kumwamba.+ 2 yokhalanso ndi anthu amphamvu ndi aatali, ana a Anaki,+ amene inu mukuwadziwa ndipo munamva anthu akunena za iwo kuti, ‘Ndani angaime pamaso pa ana a Anaki?’ 3 Ndipo inu mukudziwa bwino lero kuti Yehova Mulungu wanu akuwoloka patsogolo panu+ kuti akutsogolereni. Iye ndi moto wowononga.+ Adzawawononga+ ndipo iye ndi amene adzawagonjetsa inu mukuona. Pamenepo mudzawalande dziko lawo ndi kuwawononga mofulumira monga mmene Yehova wakuuzirani.+

4 “Yehova Mulungu wanu akadzawakankhira kutali ndi inu musadzanene mumtima mwanu kuti, ‘Yehova watilowetsa m’dziko lino kuti tilitenge kukhala lathu, chifukwa cha kulungama kwathu,’+ pamene kwenikweni Yehova akukankhira mitundu iyi kutali ndi inu chifukwa cha kuipa kwawo.+ 5 Sikuti mukulowa m’dziko ili kukalitenga kukhala lanu chifukwa cha kulungama kwanu+ kapena chifukwa cha kuwongoka mtima kwanu.+ Yehova Mulungu wanu akukankhira mitundu iyi kutali ndi inu, kwenikweni chifukwa cha kuipa kwawo,+ ndiponso kuti Yehova akwaniritse mawu onse amene analumbirira makolo anu Abulahamu,+ Isaki+ ndi Yakobo.+ 6 Muyenera kudziwa kuti Yehova Mulungu wanu akukupatsani dziko labwinoli osati chifukwa cha kulungama kwanu, pakuti ndinu anthu ouma khosi.+

7 “Kumbukirani izi: Simuyenera kuiwala mmene munaputira Yehova Mulungu wanu m’chipululu.+ Anthu inu mwasonyeza khalidwe lopandukira Yehova kuyambira tsiku limene munatuluka m’dziko la Iguputo mpaka kudzafika malo ano.+ 8 Ngakhale ku Horebe, inu munaputa mkwiyo wa Yehova moti Yehova anakukwiyirani kwambiri mpaka kufika pofuna kukufafanizani.+ 9 Nditakwera m’phiri kukalandira miyala iwiri yosema,+ miyala ya pangano limene Yehova anachita nanu,+ ndinakhala m’phirimo masiku 40, usana ndi usiku,+ (sindinadye mkate kapena kumwa madzi,) 10 ndipo Yehova anandipatsa miyala iwiri yosema imene chala cha Mulungu chinalembapo.+ Pamiyala iwiri imeneyi panali mawu onse amene Yehova analankhula nanu m’phiri, kuchokera pakati pa moto, tsiku limene munasonkhana kumeneko.+ 11 Ndipo atakwana masiku 40, usana ndi usiku, Yehova anandipatsa miyala iwiriyo, miyala ya pangano.+ 12 Pamenepo Yehova anandiuza kuti, ‘Nyamuka, tsika mofulumira m’phiri muno, chifukwa anthu ako amene unawatulutsa ku Iguputo achita zinthu zowawonongetsa.+ Apatuka mofulumira panjira imene ndinawalamula kuyendamo. Adzipangira chifaniziro chopangidwa ndi chitsulo chosungunula.’+ 13 Yehova anandiuza kuti, ‘Ndawaona anthu awa. Haa! Ndi anthu ouma khosi.+ 14 Ndileke ndiwawononge+ ndi kufafaniza dzina lawo pansi pa thambo,+ ndipo ndikupange mtundu wamphamvu ndi waukulu kwambiri kuposa iwo.’+

15 “Kenako ndinatembenuka ndi kutsika m’phirimo pamene phirilo linali kuyaka moto,+ ndipo miyala iwiri ya pangano inali m’manja mwanga.+ 16 Nditayang’ana, ndinaona kuti mwachimwira Yehova Mulungu wanu. Munali mutadzipangira mwana wa ng’ombe wachitsulo chosungunula.+ Munali mutapatuka mofulumira panjira imene Yehova anakulamulani kuyendamo.+ 17 Pamenepo ndinatenga miyala iwiriyo ndi kuiponya pansi mwamphamvu ndi manja anga, ndi kuiswa inu mukuona.+ 18 Zitatero ndinadzigwetsa pansi pamaso pa Yehova masiku 40, usana ndi usiku, ngati mmene ndinachitira poyamba. Sindinadye mkate kapena kumwa madzi+ chifukwa cha machimo anu onse amene munachita ndi kukhumudwitsa Yehova, mwa kuchita zinthu zoipa pamaso pake.+ 19 Pakuti ndinachita mantha chifukwa cha mkwiyo waukulu wa Yehova umene unakuyakirani, mpaka kufika pofuna kukufafanizani.+ Koma Yehova anandimveranso pa nthawi imeneyi.+

20 “Yehova anakwiyiranso kwambiri Aroni, mpaka kufika pofuna kumuwononga.+ Koma ine ndinapembedzeranso Mulungu+ pa nthawi imeneyo kuti asawononge Aroni. 21 Ndipo mwana wa ng’ombeyo,+ amene munachimwa pomupanga, ndinamutenga n’kumutentha ndi moto ndi kumuphwanya, n’kumupera mpaka atakhala wosalala ngati fumbi. Kenako ndinamwaza fumbilo mumtsinje wotuluka m’phirimo.+

22 “Kuwonjezera apo, pa Tabera,+ pa Masa+ ndi pa Kibiroti-hatava+ munaputanso mkwiyo wa Yehova.+ 23 Yehova atakutumani kuchokera ku Kadesi-barinea+ kuti, ‘Kwerani ndi kukatenga dziko limene ndidzakupatsani kuti likhale lanu,’ pamenepo munapandukiranso malamulo a Yehova Mulungu wanu,+ ndipo simunasonyeze chikhulupiriro+ mwa iye komanso simunamvere mawu ake.+ 24 Mwasonyeza khalidwe lopandukira Yehova+ kuyambira tsiku limene ndinakudziwani.

25 “Chotero ndinadzigwetsa pansi pamaso pa Yehova masiku 40, usana ndi usiku.+ Ndinadzigwetsa choncho chifukwa Yehova anati akufuna kukufafanizani.+ 26 Pamenepo ndinayamba kupembedzera+ Yehova ndi kunena kuti, ‘Yehova Ambuye Wamkulu Koposa, musawononge anthu anu, amene ndiwo chuma chanu chapadera,+ anthu amene munawawombola ndi mphamvu yanu, amene munawatulutsa mu Iguputo+ ndi dzanja lamphamvu.+ 27 Kumbukirani atumiki anu Abulahamu, Isaki ndi Yakobo.+ Musaone kuuma mtima kwa anthu awa ndi kuipa kwawo ndiponso tchimo lawo,+ 28 kuopera kuti anthu a m’dziko+ limene munatitulutsamo anganene kuti: “Chifukwa Yehova sanathe kuwalowetsa m’dziko limene anawalonjeza, komanso chifukwa chakuti anali kudana nawo, anawatulutsa kuti akawaphere m’chipululu.”+ 29 Iwo ndi anthu anube, chuma chanu chapadera,+ anthu amene munawatulutsa ndi mphamvu zanu zazikulu ndi dzanja lanu lotambasula.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena