Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 8:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako Nowa anamangira Yehova guwa lansembe.+ Atatero, anatenga zina mwa nyama zonse zosadetsedwa, ndi zina mwa zouluka zonse zosadetsedwa,+ nʼkuzipereka nsembe yopsereza paguwapo.+

  • Genesis 35:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno Yakobo anauza anthu a mʼbanja lake ndi onse amene anali naye kuti: “Chotsani milungu yachilendo imene ili pakati panu.+ Dziyeretseni ndipo sinthani zovala zanu. 3 Mukatero, tinyamuke tipite ku Beteli. Kumeneko ndikamangira guwa lansembe Mulungu woona, amene anandiyankha pa tsiku la kusautsika kwanga, ndipo wakhala nane kulikonse kumene ndapita.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena