Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 80:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 80 Inu Mʼbusa wa Isiraeli, mvetserani,

      Inu amene mukutsogolera Yosefe ngati gulu la nkhosa.+

      Inu amene mwakhala pampando wachifumu pamwamba* pa akerubi,+

      Onetsani kuwala kwanu.*

  • Yesaya 37:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Inu Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,+ Mulungu wa Isiraeli, wokhala pamwamba* pa akerubi, inu nokha ndinu Mulungu woona wa maufumu onse apadziko lapansi. Inuyo munapanga kumwamba ndi dziko lapansi.

  • Ezekieli 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno ulemerero wa Yehova+ unachoka pa akerubi nʼkupita pakhomo la nyumba yopatulika ndipo mtambo unayamba kudzaza nyumbayo pangʼonopangʼono.+ Komanso ulemerero wowala wa Yehova unadzaza mʼbwalo lonse la nyumbayo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena