Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Iye anapitiriza kuwagwetsera mana ngati mvula kuti adye.

      Anawapatsa tirigu wochokera kumwamba.+

      25 Anthu anadya chakudya cha amphamvu.*+

      Iye anawapatsa chakudya chokwanira.+

  • Salimo 105:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Anapempha nyama ndipo anawapatsa zinziri,+

      Ankawadyetsa chakudya chochokera kumwamba.+

  • Yohane 6:31, 32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Makolo athu anadya mana mʼchipululu,+ monga mmene Malemba amanenera kuti: ‘Anawapatsa chakudya chochokera kumwamba kuti adye.’”+ 32 Kenako Yesu anati: “Ndithudi ndikukuuzani, Mose sanakupatseni chakudya chochokera kumwamba, koma Atate wanga amakupatsani chakudya chenicheni chochokera kumwamba.

  • Yohane 6:58
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 58 Chimenechi ndi chakudya chimene chinachokera kumwamba. Nʼchosiyana ndi chakudya chimene makolo anu anadya koma nʼkumwalirabe. Aliyense wakudya chakudya chimenechi adzakhala ndi moyo wosatha.”+

  • 1 Akorinto 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano abale, ndikufuna mudziwe kuti makolo athu akale, onse anali pansi pa mtambo+ ndipo onse anawoloka nyanja.+

  • 1 Akorinto 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Onse ankadya chakudya chauzimu chofanana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena