-
Ekisodo 16:31, 32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
31 Nyumba ya Isiraeli inapatsa chakudyacho dzina lakuti “mana.”* Chinali choyera ngati mapira,* ndipo kukoma kwake kunali ngati makeke opyapyala othira uchi.+ 32 Kenako Mose anati: “Yehova walamula kuti, ‘Dzazani muyezo umodzi wa omeri ndi mana kuti asungidwe mʼmibadwo yanu yonse,+ nʼcholinga choti iwo adzaone chakudya chimene ndinakupatsani mʼchipululu nditakutulutsani mʼdziko la Iguputo.’”
-