Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 20:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako Mose anatumiza anthu kuchokera ku Kadesi kupita kwa mfumu ya Edomu+ kukanena kuti: “Abale anu Aisiraeli+ akuti, ‘Inu mukudziwa bwino za mavuto onse amene takumana nawo.

  • Numeri 20:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chonde mutilole tidutse mʼdziko lanu. Sitidutsa mʼmunda wanu uliwonse, kapena mʼmunda wa mpesa uliwonse. Sitimwa madzi apachitsime chanu chilichonse. Tizingoyenda mu Msewu wa Mfumu, osakhotera kudzanja lamanja kapena lamanzere, mpaka titadutsa mʼdziko lanu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena