Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ngati mukufuna kudya nyama, mungathe kupha chiweto chanu nʼkudya nyama yake nthawi iliyonse,+ mogwirizana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani mʼmizinda yanu yonse.* Munthu wodetsedwa komanso munthu wosadetsedwa angathe kudya nyamayo, ngati mmene mungadyere insa ndi mbawala.

  • Deuteronomo 14:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Nyama zimene mungathe kudya+ ndi izi: ngʼombe, nkhosa, mbuzi, 5 mbawala, insa, ngondo, mbuzi yakuthengo, mphalapala, nkhosa yakuthengo ndi nkhosa yamʼmapiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena