Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iye analonjeza kuti: “Inu Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, mukaona kuvutika kwa ine kapolo wanu nʼkundikumbukira ndiponso mukapanda kundiiwala ine kapolo wanu nʼkundipatsa mwana wamwamuna,+ ndidzamʼpereka kwa Yehova masiku onse a moyo wake ndipo lezala silidzadutsa mʼmutu mwake.”+

  • 1 Samueli 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako Elikana anapita kunyumba kwake ku Rama, koma mwanayo anatsala nʼkumatumikira Yehova+ moyangʼaniridwa ndi wansembe Eli.

  • 2 Mbiri 31:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kuwonjezera pamenepo, ankagawiranso amuna oyambira zaka zitatu kupita mʼtsogolo amene anali pamndandanda wa mayina wotsatira makolo awo. Amuna amenewa ankabwera tsiku ndi tsiku kudzatumikira kunyumba ya Yehova komanso kudzagwira ntchito ya magulu awo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena