-
2 Samueli 22:31Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Iye ndi chishango kwa onse othawira kwa iye.+
-
-
Salimo 27:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Ngakhale nkhondo yolimbana ndi ine itayambika,
Pameneponso ndidzadalira Mulungu.
-
-
Salimo 118:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Mitunduyo inandizungulira, ndithu inandizungulira kumbali zonse.
Koma mʼdzina la Yehova
Ndinaithamangitsira kutali.
-