Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 39:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndithudi, mwachepetsa masiku a moyo wanga,+

      Ndipo masiku a moyo wanga si kanthu pamaso panu.+

      Ndithudi, munthu aliyense ngakhale ataoneka kuti ndi wotetezeka, amangokhala ngati mpweya.+ (Selah)

       6 Zoonadi, moyo wa munthu aliyense umangodutsa ngati chithunzithunzi.

      Iye amangovutika* popanda phindu.

      Amaunjika chuma, osadziwa kuti amene adzasangalale nacho ndi ndani.+

  • Yakobo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mumanena zimenezi chonsecho simukudziwa kuti moyo wanu udzakhala wotani mawa.+ Chifukwa muli ngati nkhungu imene imangooneka kwa kanthawi kochepa kenako nʼkuzimiririka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena