Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 29:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ifetu ndife alendo pamaso panu, komanso okhala mʼdziko la eni ngati mmene analili makolo athu onse.+ Masiku athu padziko lapansi ali ngati mthunzi+ ndipo ndife osakhalitsa.

  • Salimo 102:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Masiku a moyo wanga ali ngati chithunzithunzi chimene chimazimiririka,+

      Ndipo ndafota ngati udzu.+

  • Salimo 144:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Munthu amafanana ndi mpweya.+

      Masiku a moyo wake ali ngati mthunzi wongodutsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena