Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kwatsala kanthawi kochepa, ndipo oipa sadzakhalaponso.+

      Udzayangʼana pamene ankakhala,

      Ndipo sadzapezekapo.+

  • Salimo 92:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anthu oipa akaphuka ngati msipu

      Ndipo anthu onse ochita zoipa zinthu zikamawayendera bwino,

      Zimatero kuti awonongedwe kwamuyaya.+

  • Yakobo 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Dzuwa likatuluka limatentha kwambiri nʼkufotetsa zomera ndipo maluwa a zomerazo amathothoka moti kukongola kwake kumatha. Mofanana ndi zimenezi munthu wachumayo adzafa ali mkati mofunafuna chuma.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena