Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 15:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Samueli anati: “Kodi Yehova amasangalala ndi nsembe zopsereza ndi nsembe zina+ kuposa kumvera mawu a Yehova? Dikira ndikuuze! Kumvera kumaposa nsembe,+ ndipo kumvetsera mosamala kumaposa mafuta+ a nkhosa zamphongo.

  • Salimo 40:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Nsembe zanyama komanso nsembe zina, simunazifune.*+

      Koma munatsegula makutu anga kuti ndimve.+

      Simunapemphe nsembe zopsereza ndi nsembe zamachimo.+

  • Hoseya 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Chifukwa ndimakondwera ndi chikondi chokhulupirika,* osati nsembe.

      Ndimakondweranso ndi kudziwa Mulungu, osati nsembe zopsereza zathunthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena