Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Adzaopa ndipo adzagwidwa ndi mantha aakulu.+

      Chifukwa cha dzanja lanu lamphamvu, adzakhala ngati mwala, osachita kanthu.

      Mpaka anthu anu atadutsa, inu Yehova,

      Mpaka anthu anu amene munawapanga+ atadutsa.+

  • Salimo 76:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mulungu adzachititsa manyazi atsogoleri onyada.

      Iye amachititsa kuti mafumu apadziko lapansi akhale ndi mantha.

  • Yesaya 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Anthu adzalowa mʼmapanga a muthanthwe

      Ndiponso mʼmayenje a munthaka,+

      Chifukwa cha kuopsa kwa mkwiyo wa Yehova

      Ndiponso chifukwa cha ulemerero wake waukulu+

      Akaimirira kuti achititse dziko lapansi kunjenjemera ndi mantha.

  • Yeremiya 10:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Yehova ndi Mulungu woonadi.

      Iye ndi Mulungu wamoyo+ ndipo ndi Mfumu yamuyaya.+

      Dziko lapansi lidzagwedezeka chifukwa cha mkwiyo wake,+

      Ndipo palibe mitundu ya anthu imene idzapilire mkwiyo wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena