Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kodi ndiyenera kudya nyama ya ngʼombe zamphongo

      Kapena kumwa magazi a mbuzi?+

      14 Yamikani Mulungu kuti ikhale ngati nsembe imene mukupereka kwa iye,+

      Ndipo perekani kwa Wamʼmwambamwamba zimene mwalonjeza.+

      15 Pa nthawi yamavuto mundiitane.+

      Ine ndidzakupulumutsani, ndipo inu mudzandilemekeza.”+

  • Hoseya 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Bwererani kwa Yehova ndi mawu amenewa.

      Uzani Mulungu kuti, ‘Tikhululukireni zolakwa zathu.+ Landirani zinthu zathu zabwino,

      Ndipo tidzakutamandani ndi pakamwa pathu+ ngati mmene tingaperekere nsembe kwa inu ana a ngʼombe amphongo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena