Salimo 89:36, 37 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Mbadwa* zake zidzakhalapo mpaka kalekale,+Ndipo mpando wake wachifumu udzakhala pamaso panga kwamuyaya ngati dzuwa.+ 37 Udzakhalapo mpaka kalekale ngati mweziUdzakhala ngati mboni yokhulupirika yamumlengalenga.” (Selah) Luka 1:32, 33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Ameneyu adzakhala wamkulu+ ndipo adzatchedwa Mwana wa Wamʼmwambamwamba.+ Yehova* Mulungu adzamupatsa mpando wachifumu wa Davide atate wake.+ 33 Iye adzalamulira monga Mfumu panyumba ya Yakobo kwamuyaya ndipo Ufumu wake sudzatha.”+ Chivumbulutso 11:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Mngelo wa 7 analiza lipenga lake.+ Ndiyeno kumwamba kunamveka mawu osiyanasiyana akunena mokweza kuti: “Ufumu wa dziko wakhala Ufumu wa Ambuye wathu+ ndi wa Khristu wake+ ndipo iye adzalamulira monga mfumu mpaka kalekale.”+
36 Mbadwa* zake zidzakhalapo mpaka kalekale,+Ndipo mpando wake wachifumu udzakhala pamaso panga kwamuyaya ngati dzuwa.+ 37 Udzakhalapo mpaka kalekale ngati mweziUdzakhala ngati mboni yokhulupirika yamumlengalenga.” (Selah)
32 Ameneyu adzakhala wamkulu+ ndipo adzatchedwa Mwana wa Wamʼmwambamwamba.+ Yehova* Mulungu adzamupatsa mpando wachifumu wa Davide atate wake.+ 33 Iye adzalamulira monga Mfumu panyumba ya Yakobo kwamuyaya ndipo Ufumu wake sudzatha.”+
15 Mngelo wa 7 analiza lipenga lake.+ Ndiyeno kumwamba kunamveka mawu osiyanasiyana akunena mokweza kuti: “Ufumu wa dziko wakhala Ufumu wa Ambuye wathu+ ndi wa Khristu wake+ ndipo iye adzalamulira monga mfumu mpaka kalekale.”+