Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kwatsala kanthawi kochepa, ndipo oipa sadzakhalaponso.+

      Udzayangʼana pamene ankakhala,

      Ndipo sadzapezekapo.+

  • Salimo 37:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma oipa onse adzatheratu,+

      Adani a Yehova adzasowa mofulumira ngati malo okongola odyetsera ziweto amene msipu wake wobiriwira suchedwa kufota.

      Iwo adzatha mofulumira ngati utsi.

  • Salimo 55:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma inu Mulungu, mudzatsitsira oipawo mʼdzenje lakuya.+

      Anthu amene ali ndi mlandu wa magazi komanso achinyengowo, sadzakwanitsa kukhala ngakhale hafu ya moyo wawo.+

      Koma ine ndidzakhulupirira inu.

  • Miyambo 3:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Yehova amatemberera banja la munthu woipa,+

      Koma iye amadalitsa nyumba ya munthu wolungama.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena