2 Iye amandisonyeza chikondi chake chokhulupirika ndipo ndi malo anga otetezeka,
Malo anga othawirako otetezeka komanso amene amandipulumutsa,
Chishango changa ndiponso malo amene ndathawirako kuti nditetezeke,+
Amene amachititsa kuti mitundu ya anthu izindigonjera.+