Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 92:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndipo adzalengeza kuti Yehova ndi wolungama.

      Iye ndi Thanthwe langa,+ ndipo sachita zosalungama.

  • Salimo 119:68
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 68 Inu ndinu wabwino+ ndipo ntchito zanu ndi zabwino.

      Ndiphunzitseni malamulo anu.+

  • Salimo 145:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova ndi wabwino kwa aliyense,+

      Ndipo ntchito zake zonse zimasonyeza kuti ndi wachifundo.

  • Machitidwe 14:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Komabe iye sanangokhala wopanda umboni+ wakuti anachita zabwino. Anakupatsani mvula kuchokera kumwamba ndi nyengo zimene zokolola zanu zimakhala zambiri.+ Anadzaza mitima yanu ndi chakudya komanso chisangalalo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena