Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pa tsiku lachitatu mʼmawa, kunachita mabingu ndi mphezi ndipo mtambo wakuda+ unakuta phiri. Kunamvekanso kulira kwamphamvu kwambiri kwa lipenga la nyanga ya nkhosa, moti anthu onse mumsasawo anayamba kunjenjemera.+

  • Ekisodo 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Phiri la Sinai linafuka utsi paliponse, chifukwa chakuti Yehova anabwera paphiripo mʼmoto.+ Utsi wakewo unkakwera kumwamba ngati utsi wa uvuni ndipo phiri lonse linkanjenjemera kwambiri.+

  • Salimo 77:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Phokoso la bingu lanu+ linali ngati la mawilo a galeta.

      Kungʼanima kwa mphezi kunaunika padziko lapansi.+

      Dziko lapansi linanjenjemera komanso kugwedezeka.+

  • Salimo 104:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Amayangʼana dziko lapansi ndipo limanjenjemera.

      Amagwira mapiri ndipo amafuka utsi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena